Home Uncategorized Bambo amangidwa chifukwa chomenya mkazi wake ndi chitsulo.

Bambo amangidwa chifukwa chomenya mkazi wake ndi chitsulo.

by lovecomradio@gmail.com
0 comments

Wolemba Alice Lissa Kamwanje.

Apolisi m’boma la Salima amanga bambo wa zaka 24 zakubadwa a Kumbukani Wedi chifukwa chovulaza mkazi wawo zomwe zapangitsa a chipatala kuchotsa diso lake kamba kovulala.

Mneneri wa apolisi m’bomali Sub Inspector Rabecca Ndiwate wati bamboyu anamenya mkazi wake pomukaikira ndikomwe anatenga ndalama yogulira koilo.

A Ndiwate wati bamboyu anamumenya mkaziyu m’maso ndi chitsulo zomwe zinapangitsa kuti avulale kwambiri diso.

Pakadali pano apolisi alimbikitsa anthu omwe akukumana ndi nkhaza kuti azikanena ku polisi Kuti apeze thandizo ndi upangiri pofuna kuchepetsa nkhaza.

A Kumbukani Wedi amachokera m’mudzi wa Ntochera mfumu yaikulu Pemba m’boma la Salima.

You may also like

Leave a Comment

Love FM is a licensed Malawian community radio station with a 107.6 frequency established to provide high quality,proffessional and reliable information services in community radio broadcasting that exceeds the expectations of people living in communities.

It is a tool of communication in Salima district to facilitate issues of Climate change and environment,education, gender-based violence, culture, child trafficking, Agriculture, transparency and accountability, sports, community self reliance, and many more.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00