Home Featured Amangidwa atapezeka ndi Chamba.

Amangidwa atapezeka ndi Chamba.

by lovecomradio@gmail.com
2 comments

Wolemba William Chitengu Jnr

A Polisi m’boma la Salima amanga abambo atatu kamba kopezeka ndi chamba opanda chilorezo.

Malingana ndi Mneneri wa polisi ya Salima, Sub inspector Rabecca ndiwate abambo atatuwa agwidwa usiku wapa 25/26 April 2025 pamene apolisi anaika malo ochitira chipikisheni pafupi ndi malo omwetsera mafuta a mlamba mseu wa Salima-Balaka.

Oganiziridwa oyamba a Mickson Thomson azaka 37, awanga potsatira a polisi kufufuza galimoto yomwe amayendera ndipo anapeza thumba lomwe munali chambachi.

A Mathews Mafuta a zaka 40, komanso a Happy Chiumia a zaka 27, amangidwa pamene amafuna kuzembetsa chambachi pogwiritsa ntchito njinga za moto.

Atatuwa akaonekera ku bwalo la milandu posachedwapa pamene akayankhe milandu yokhudza nkhaniyi.

You may also like

2 comments

Jerry300 April 27, 2025 - 1:40 am

Very good https://t.ly/tndaA

Reply
Janet2140 April 27, 2025 - 10:20 am

Very good https://t.ly/tndaA

Reply

Leave a Comment

Love FM is a licensed Malawian community radio station with a 107.6 frequency established to provide high quality,proffessional and reliable information services in community radio broadcasting that exceeds the expectations of people living in communities.

It is a tool of communication in Salima district to facilitate issues of Climate change and environment,education, gender-based violence, culture, child trafficking, Agriculture, transparency and accountability, sports, community self reliance, and many more.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00