Home Uncategorized SADFA ili ndi adindo atsopano.

SADFA ili ndi adindo atsopano.

by lovecomradio@gmail.com
0 comments

Chithunzi Adams Cuba Phiri.

Wolemba Liana Bonongwe

Adams Curba Phiri ndiye wapambana pa udindo wa wapampando wa Salima district football association (SADFA) atagonjetsa yemwe anali wapampando wabungweri Abdul Salaam Mtimbwinda ndi ma vote 33 kwa 9.

Chisankhochi chachitika loweluka ku Matenje Teachers Development Center (TDC) pomwe nthumwi zotsatira masewero a Mpira kuchokera muma zone onse a m’boma anaponya vote.

Sheikh Ibrahim Omar ndi amene apambana pa udindo wa wachiwiri kwa wapampando opanda opikisana naye.

Mu mkuyankhula kwake atapambana Phiri wati agwira ntchito ndi aliyese pofuna kupititsa patsogolo mpira m’boma la Salima.

Iye wati ali ndi masomphenya obweletsa team ya Nyasa Big bullets kuzakumana ndi team yochokera m’boma la Salima pamene Bwalo la zamasewero la Community lizidzatsegulidwa.

You may also like

Leave a Comment

Love FM is a licensed Malawian community radio station with a 107.6 frequency established to provide high quality,proffessional and reliable information services in community radio broadcasting that exceeds the expectations of people living in communities.

It is a tool of communication in Salima district to facilitate issues of Climate change and environment,education, gender-based violence, culture, child trafficking, Agriculture, transparency and accountability, sports, community self reliance, and many more.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00

Connection Information

To perform the requested action, WordPress needs to access your web server. Please enter your FTP credentials to proceed. If you do not remember your credentials, you should contact your web host.

Connection Type